14. Mwa ici anena, Khala maso wogona iwe, nuuke kwa akufa, ndi, po Kristu adzawala pa iwe.
15. Potero, penyani bwino umo muyendera, si monga opanda nzeru, koma monga anzeru;
16. akucita macawi, popeza masiku ali oipa,
17. Cifukwa cace musakhale opusa, koma dziwitsani cifuniro ca Ambuye nciani.
18. Ndipo musaledzere naye vinyo, m'mene muli citayiko; komatu mudzale naye Mzimu,