2 Timoteo 4:12-15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

12. Koma Tukiko ndamtuma ku Efeso.

13. Copfunda cija ndinacisiya ku Trowa kwa Karpo, udze naco pakudza iwe, ndi mabuku, makamaka zikopa zija zolembedwa.

14. Alesandro wosula mkuwa anandicitira zoipa zambiri: adzambwezera iye Ambuye monga mwa nchito zace;

15. ameneyo iwenso ucenjere naye; pakuti anatsutsana nao mau athu.

2 Timoteo 4