2 Samueli 5:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma pamene Afilisti anamva kuti adamdzoza Davide mfumu ya Israyeli, Afilisti onse anakwera kukafuna Davide; ndipo Davide anacimva natsikira kungaka kuja.

2 Samueli 5

2 Samueli 5:16-25