2 Samueli 21:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Naika mafupa a Sauli ndi Jonatani mwana wace ku dziko la Benjamini m'Zela, m'manda a Kisi atate wace; nacita zonse inalamulira mfumu. Ndipo pambuyo pace Mulungu anapembedzeka za dzikolo.

2 Samueli 21

2 Samueli 21:5-15