2 Samueli 19:41 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo onani, Aisrayeli onse anafika kwa mfumu, nanena ndi mfumu, Abale athu anthu a Yuda anakucotsani bwanji mwakuba, naolotsa mfumu ndi banja lace pa Yordano, ndi anthu onse a Davide pamodzi naye?

2 Samueli 19

2 Samueli 19:35-43