2 Samueli 19:32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Barizilai anali nkhalamba, ndiye wa zaka makumi asanu ndi atatu; ndiye amene anapereka cakudya kwa mfumu muja anagona ku Mahanaimu, pakuti anali munthu womveka ndithu.

2 Samueli 19

2 Samueli 19:22-38