2 Samueli 19:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nati kwa mfumu, Mbuye wanga asandiwerengere ine mphulupulu ndiponso musakumbukile cimene mnyamata wanu ndinacita mwamphulupulu tsiku lila mbuye wanga mfumu anaturuka ku Yerusalemu, ngakhale kucisunga mumtima mfumu.

2 Samueli 19

2 Samueli 19:13-28