2 Samueli 19:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anali nao anthu cikwi cimodzi Abenjamini, ndi Ziba mnyamata wa nyumba ya Saul; ndi ana ace amuna khumi ndi asanu, ndi anyamata ace makumi awiri pamodzi naye; iwo naoloka Yordano pamaso pa mfumu.

2 Samueli 19

2 Samueli 19:12-25