2 Samueli 18:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yoabu ananena ndi womuuzayo, Ndipo taona, unamuona, tsono unalekeranji kumkantha agwe pansi pomwepo? ndipo ine ndikadakupatsa ndarama khumi ndi lamba.

2 Samueli 18

2 Samueli 18:7-20