2 Samueli 17:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Ahitofeli, pakuona kuti sautsata uphungu wace anamanga buru wace, nanyamuka, nanka kumudzi kwao, nakonza za pa banja lace, nadzipacika, nafa, naikidwa m'manda a atate wace.

2 Samueli 17

2 Samueli 17:22-25