2 Samueli 16:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Husai nanena ndi Abisalomu, lai; koma amene Yehova anasankha ndi anthu awa, ndi anthu onse a Israyeli, ine ndiri wace, ndipo ndidzakhala naye iyeyu.

2 Samueli 16

2 Samueli 16:17-20