2 Samueli 15:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Abisalomu anatinso, Mwenzi atandiika ine ndikhale woweruza m'dzikomo, kuti munthu yense amene ali ndi mrandu wace kapena cifukwa cace, akadafika kwa ine; ndipo ndikadamcitira zacilungamo!

2 Samueli 15

2 Samueli 15:1-14