2 Samueli 15:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anyamata ace onse anapita naye limodzi; ndi Akereri ndi Apeleti, ndi Agiti onse, anthu mazana asanu ndi limodzi omtsata kucokera ku Gati, anapita pamaso pa mfumu.

2 Samueli 15

2 Samueli 15:8-27