2 Samueli 14:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mkaziyo anati, Cifukwa ninjinso munalingalira cinthu cotere pa anthu a Mulungu? pakuti pakulankhula mau awa mfumu ikunga woparamula, popeza mfumu siitumiza okamtenganso woingidwa wace.

2 Samueli 14

2 Samueli 14:12-23