2 Samueli 10:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Aaramu anathawa pamaso pa Israyeli; Davide naphapo Aaramu apamagareta mazana asanu ndi awiri, ndi apakavalo zikwi makumi anai, nakantha Sobaki kazembe wa khamu lao, nafa iye pomwepo.

2 Samueli 10

2 Samueli 10:12-19