2 Mbiri 36:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndiponso anapandukana naye mfumu Nebukadinezara, amene adamlumbiritsa pa Mulungu; koma anaumitsa khosi lace, nalimbitsa mtima wace kusatembenukira kwa Yehova Mulungu wa Israyeli,

2 Mbiri 36

2 Mbiri 36:12-22