2 Mafumu 4:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo linafika tsiku lakuti Elisa anapitirira kumka ku Sunemu, kumeneko kunali mkazi womveka; ameneyo anamuumiriza adye mkate. Potero pomapitirako iyeyu, adafowapa, mbukirako kukadya mkate.

2 Mafumu 4

2 Mafumu 4:3-9