2 Mafumu 4:35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo anabwera nayenda m'nyumba, cakuno kamodzi, cauko kamodzi; nakwera, nadzitambasuliranso pa iye; ndi mwana anayetsemula kasanu ndi kawiri, natsegula mwanayo maso ace.

2 Mafumu 4

2 Mafumu 4:29-41