2 Mafumu 4:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Timmangire kacipinda kosanja, timuikirenso komweko kama, ndi gome, ndi mpando, ndi coikapo nyali; ndipo kudzatero kuti akatidzera alowe m'mwemo.

2 Mafumu 4

2 Mafumu 4:5-20