2 Mafumu 3:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Elisa anati, Pali Yehova wa makamu, amene ndiima pamaso pace, ndikadapanda kusamalira nkhope ya Yehosafati mfumu ya Yuda, sindikadakuyang'anitsani, kapena kukuonani.

2 Mafumu 3

2 Mafumu 3:4-19