2 Mafumu 25:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo linga la mudziwo linagamulidwa, nathawira ankhondo onse usiku, njira ya ku cipata ca pakati pa makoma awiri, iri ku munda wa mfumu; Akasidi tsono anali pamudzi pouzinga; nimuka mfumu pa njira ya kucidikha.

2 Mafumu 25

2 Mafumu 25:1-8