2 Mafumu 23:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nacotsanso akavalo amene mafumu a Yuda adapereka kwa dzuwa, polowera nyumba ya Yehova, ku cipinda ca Natani Meleki mdindoyo, cokhala kukhonde; natentha magareta a dzuwa ndi moto.

2 Mafumu 23

2 Mafumu 23:10-15