2 Mafumu 2:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo amuna a kumudzi anati kwa Elisa, Taonani, pamudzi pano mpabwino, monga umo aonera mbuye wanga; koma madzi ndi oipa, ndi nthaka siibalitsa.

2 Mafumu 2

2 Mafumu 2:17-23