2 Mafumu 2:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunacidka, akali ciyendere ndi kukambirana, taonani, anaoneka gareta wamoto ndi akavalo amoto, nawalekanitsa awiriwa; Eliya nakwera kumwamba ndi kabvumvulu.

2 Mafumu 2

2 Mafumu 2:6-13