2 Mafumu 19:35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali, usiku womwewo mthenga wa Yehova anaturuka, nakantha m'misasa ya Aasuri zikwi zana limodzi mphambu makumi asanu ndi atatu kudza zisanu, ndipo pouka anthu mamawa, taonani, onsewo ndi mitembo.

2 Mafumu 19

2 Mafumu 19:25-37