2 Mafumu 17:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ana a Israyeli anacita m'tseri zinthu zosayenera pa Yehova Mulungu wao, nadzimangira misanje m'midzi mwao monse ku nsanja ya olonda ndi ku mudzi walinga komwe.

2 Mafumu 17

2 Mafumu 17:1-15