2 Mafumu 17:29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma a mtundu uli wonse anapanga milungu yao yao, naiika m'nyumba za misanje adazimanga Asamariya, a mtundu uli wonse m'midzi mwao mokhala iwo.

2 Mafumu 17

2 Mafumu 17:21-31