2 Mafumu 16:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nthawi yomweyo Rezini mfumu ya Aramu anabwezera Elati kwa Aramu, napitikitsa Ayuda ku Elati; nadza Aaramu ku Elati, nakhala komweko kufikira lero lino.

2 Mafumu 16

2 Mafumu 16:1-16