2 Mafumu 10:29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Yehu sanazileka zoipa za Yerobiamu mwana wa Nebati, zimene adacimwitsa nazo Israyeli, ndizo ana a ng'ombe agolidi okhala m'Beteli ndi m'Dani.

2 Mafumu 10

2 Mafumu 10:27-36