2 Mafumu 10:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nati iye, Agwireni amoyo. Nawagwira amoyo, nawapha ku dzenje la nyumba yosengera, ndiwo amuna makumi anai mphambu awiri; sanasiya ndi mmodzi yense.

2 Mafumu 10

2 Mafumu 10:13-15