2 Atesalonika 2:3-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. munthu asakunyengeni konseko; kuti silifika, koma ciyambe cifike cipatukoco, nabvumbulutsike munthu wosayeruzika, mwana wa cionongeko,

4. amene atsutsana nazo, nadzikuza pa zonse zochedwa Mulungu, kapena zopembedzeka; kotero kuti iye wakhalapansi ku Kacisi wa Mulungu, nadzionetsera yekha kuti ali Mulungu.

5. Simukumbukila kodi, kuti pokhala nanu, ndisanacoke ine, ndinakuuzani izi?

2 Atesalonika 2