2 Akorinto 9:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iye wopatsa mbeu kwa wofesa, ndi mkate ukhale cakudya, adzapatsa ndi kucurukitsa mbeu yanu yofesa, nadzaonjezapo pa zipatso za cilungamo canu;

2 Akorinto 9

2 Akorinto 9:4-13