2 Akorinto 5:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Sitidzibvomeretsanso ife tokha kwa inu, koma tikupatsani inu cifukwa ca kudzitamandira pa ife, kuti mukakhale nako kanthu kakutsutsana nao iwo akudzitamandira pooneka pokha, osati mumtima.

2 Akorinto 5

2 Akorinto 5:7-16