2 Akorinto 4:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti Mulungu amene anati, Kuunika kudzawala kuturuka mumdima, ndiye amene anawala m'mitima yathu kutipatsa ciwalitsiro ca cidziwitso ca ulemerero wa Mulungu pankhope pa Yesu Kristu.

2 Akorinto 4

2 Akorinto 4:5-14