2 Akorinto 2:10-12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

10. Koma amene mumkhululukira kanthu, inenso nditero naye; pakuti cimene ndakhululukira inenso, ngati ndakhululukira kanthu, ndacicita cifukwa ca inu, pamasopa Kristu;

11. kuti asaticenierere Satana; pakuti sitikhala osadziwa macenjerero ace.

12. Koma pamene ndinadza ku Trowa kudzalalikira Uthenga Wabwino wa Kristu, ndipo pamene padanditsegukira kwa ine pakhomo, mwa Ambuye,

2 Akorinto 2