2 Akorinto 11:32-33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

32. M'Damasiko kazembe wa mfumu Areta analindizitsa mudzi wa Adamasiko kuti andigwire ine;

33. ndipo mwa zenera, mumtanga, ananditsitsa pakhoma, ndipo ndinapulumuka m'manja mwace.

2 Akorinto 11