2 Akorinto 10:3-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Pakuti pakuyendayenda m'thupi, siticita nkhondo monga mwa thupi,

4. (pakuti zida za nkhondo yathu siziri za thupi, koma zamphamvu mwa Mulungu zakupasula malinga);

5. ndi kugwetsa matsutsano, ndi cokwezeka conse cimene cidzikweza pokana ddziwitso ca Mulungu, ndi kugonjetsa ganizo lonse ku kumvera kwa Kristu;

2 Akorinto 10