1 Yohane 5:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Wina akaona mbale wace alikucimwa cimo losati la kuimfa, apemphere Mulungu, ndipo iye adzampatsira moyo wa iwo akucita macimo osati a kuimfa. Pali cimo la kuimfa: za ililo sindinena kuti mupemphere.

1 Yohane 5

1 Yohane 5:8-21