1 Yohane 5:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yense wokhulupirira kuti Yesu ndiye Kristu wabadwa kucokera kwa Mulungu; ndipo yense wakukonda iye amene anabala akondanso iye amene anabadwa wocokera mwa iye.

1 Yohane 5

1 Yohane 5:1-11