1 Yohane 2:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Tiana tanga, izi ndikulemberani, kuti musacimwe. Ndipo akacimwa wina, Nkhoswe tiri naye kwa Atate, ndiye Yesu Kristu wolungama;

2. ndipo iye ndiye ciombolo ca macimo athu; koma wosati athu okha, komanso a dziko lonse lapansi.

3. Ndipo umo tizindikira kuti tamzindikira iye, ngati tisunga malamulo ace.

1 Yohane 2