1 Yohane 1:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ngati tibvomereza macimo athu, ali wokhulupirika ndi wolungama iye, kuti atikhululukire macimo athu, ndi kutisambitsa kuticotsera cosalungama ciri conse.

1 Yohane 1

1 Yohane 1:1-10