13. Pakuti Adamu anayamba kulengedwa, pamenepo Heva;
14. ndipo Adamu sananyengedwa, koma mkaziyo ponyengedwa analowa m'kulakwa;
15. koma adzapulumutsidwa mwa kubala mwana, ngati akhala m'cikhulupiriro ndi cikondi ndi ciyeretso pamodzi ndi cidziletso.