1 Samueli 8:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova ananena ndi Samueli, Umvere mau onse anthuwo alikulankhula nawe; popeza sindiwe anakukana, koma ndine anandikana, kuti ndisakhale mfumu yao.

1 Samueli 8

1 Samueli 8:1-13