1 Samueli 30:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

nampatsanso cigamphu ca ncinci ya nkhuyu ndi ncinci ziwiri za mphesa; ndipo atadya, moyo wace unabweranso mwa iye; pakuti adagona masiku atatu ndi usiku wao, osadya cakudya, osamwa madzi.

1 Samueli 30

1 Samueli 30:9-19