1 Samueli 3:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Popeza ndinamuuza kuti ndidzaweruza nyumba yace kosatha cifukwa ca zoipa anazidziwa, popeza ana ace anadzitengera temberero, koma iye sanawaletsa.

1 Samueli 3

1 Samueli 3:7-16