1 Samueli 28:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsono Sauli anati kwa anyamata ace, Mundifunire mkazi wobwebweta, kuti ndimuke kwa iye ndi kumfunsira. Ndipo anyamata ace anati kwa iye, Onani ku Endori kuli mkazi wobwebweta.

1 Samueli 28

1 Samueli 28:3-17