1 Samueli 24:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehova aweruze pakati pa ine ndi inu; ndipo Yehova adzandibwezera cilango kwa inu; koma dzanja langa silidzakhala pa inu.

1 Samueli 24

1 Samueli 24:8-20