1 Samueli 21:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo wansembeyo anayankha Davide nati, Ndiribe mkate wacabe, koma ulipo mkate wopatulika; pokhapo ngati anyamatawo anadzisunga kupewa akazi.

1 Samueli 21

1 Samueli 21:1-6