1 Samueli 21:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nati Davide kwa Ahimeleki wansembeyo, Mfumu inandilamulira nchito, ninena nane, Asadziwe munthu ali yense kanthu za nchito imene ndakutumira ndi kukulamulira; ndipo ndawapanga anyamatawo ku malo akuti.

1 Samueli 21

1 Samueli 21:1-7