1 Samueli 21:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anyamata a Akisi ananena naye, Uyu si Davide mfumu ya dzikolo kodi? Sanathirirana mang'ombe za iye kodi m'magule ao, ndi kuti,Sauli anapha zikwi zace,Koma Davide zikwi zace zankhani?

1 Samueli 21

1 Samueli 21:9-15